This snapshot, taken on 03/08/2004, shows web content selected for preservation by The National Archives. External links, forms and search boxes may not work in archived websites.

Investigating bilingual literacy: Evidence from Malawi and Zambia - Education Research Paper No. 24, 1998, 99 p.

[Previous Page] [Table of Contents]

Appendix I - Text for Chichewa/Nyanja individual reading

Mfumu Mitulo atacoka pamudzi paja nyakwawa Kameta ndi anthu ake pamodzi ndi ena ocokera m'midzi yozungulira, anagundika nayo nchito youmba ncherwa zomangira sukulu.

Azimai ndiwo amabweretsa madzi ndi udzu wophimba pancherwa, pamene anyamata anali kuthamanga ndi zikombole. Azibambo ndiwo anali m'nkhando kumaponda dothi. Panthawiyi amuna ena anali kudula nkhuni zodzatenthera ncherwa.

Ncherwa zittakonzedwa, nyakwawa Kameta anauza Bambo Jamu omwe amadziwa kamangidwe ke nyumba za ncherwa kuti akayambeko kukumba maziko a sukulu.

[Previous Page] [Top of Page]