|
Report on reading in English in primary schools in Zambia - Education Research Paper No. 05, 1993, 55 p. [Previous Page] [Table of Contents] [Next Page] Appendix F - Nyanja reading test: ExtractsV.01 Dzina.............................. Tsiku lobadwa............................. Ndime Yophunzirira Mpira
Ana atatu ali kusewela ndi mpira ________. Siwa ali kuponyera ________ kwa Simon. Iye awungwira ________ kuponyera kwa Maria. Onse ________ kusewela ndi mpira. Atate ace a Mumbi
Atate ace a Mumbi ndi mlimi. Ali ndi dimba lalikulu. Liri pafupi ndi mudzi wawo. Matsiku onse amauka ________ ndi kuyenda ________ kwao. Amalima nyemba, ________ mdi cimanga cabiri. Mumbi ________ kudimba. Miriamu
Miriam ali ndi zaka khumi. Ali ndi mung'ono wace wamwamuna ndi wamkazi. ________ mu ________ kakang'ono ndi amai ndi ________ awo. Matsiku onse Miriam ndi mung'ono wace wamwamuna ________ kusukulu. Mung'ono wace ________ Jelita ali ndi zaka ziwiri. kusukulu. Atate ace a Sifo
Atae ace a Sifo ali ndi ng'ombe ________ ndi mbuzi zisanu ndi ziwiri. Ng'ombe ndi ________ za mawanga akuda ndi. ________ ndi zakatondo. Simadya ________ ndi kumwa akumsinje. Tsiku loweruka, pamene Sifo ________ ku sukulu, amaziyang'anira. Mabvuto ndi njinga yace
Mabvuto akuyendetsa njinga yace ________. Ali ________ ku sitoro kukagula ________. Pali galu pabwalo mwa ________ ya nyumbazo.
Ngati yawona Mabvuto ________ kumuthamangitsa. Basiketi ya mabvuto yagwa ________. Mzimai atuluka mnyumba ndi ________ galu. Ndipo atenga ________ ndikumupatsa Mabvuto.
|